Police in Chiradzulu District have arrested two men on suspicion that they murdered 47-year-old Yohane Arnold and robbed Blessings Muleriwa, a local businessman at Malindi...
Khoti lina m’boma la Phalombe lalamula a Paul Mwina a zaka 35 zakubadwa kuti akagwire jele kwa zaka 14 chifukwa adagwililira mwana omupeza wazaka 12...
Khothi la Magistrate ku Blantyre lalamula amuna awiri ndi mayi m’modzi kuti apereke chindapusa pa milandu yosiyanasiyana yomwe anapalamula. Anthuwa ndi a Chifundo Kauwa, 38,...
Eleven suspected members of a notorious group of youths called ‘B13’ are behind bars for allegedly disturbing classes at schools around Soche area in Blantyre....
Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000. M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati...
Khoti la Magistrate ku Phalombe lalamula nyakwawa Nayuma, yomwe dzina lake ndi Leonard Julius, kukakhala kundende zaka 12 chifukwa chogwililira mtsikana wazaka 14. Mneneri wapolisi...
Bwalo la milandu m’boma la Mangochi lalamula a Nelson Lipenga kuti akagwire ukaidi wa kalavula gaga kwa zaka makumi awiri (20) kaamba kopezeka olakwa pa...
The Senior Magistrate Court in Mangochi has ordered Mary Julius Saidi,24 and Molly Kainga,34 to pay fines after they were convicted on six counts each...
Lilongwe Police Station has detained two individuals on suspicion that they orchestrated a fraudulent scheme, resulting in the loss of K750,000 by a local businessman....