Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Related posts

Airtel Malawi enhances security to combat mobile money fraud

Rabson Kondowe

Livingstonia Synod commends government’s development efforts

Romeo Umali

Amabera anthu powanamiza kuti amachulukitsa ndalama

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.