Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Related posts

Bullets vs Eagles at BNS

Romeo Umali

Malawi U-17 girls out of COSAFA Cup

Romeo Umali

Malawi set to host ANOCA Zone VI Elective AGM

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.