Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Alimi apeza misika ya ndalama zochuluka kuchiwonetsero chazaulimi

Justin Mkweu

Gender Ministry highlights importance of reporting on social protection programmes

MBC Online

JZU’S  LEGACY INDELIBLE

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.