Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Boma likuyesetsa kutulutsa ma Passport — Zikhale Ng’oma

Nduna yoona chitetezo cha m’dziko, a Ken Zikhale Ng’oma, yati ziphaso zolowera ndi kutulukira m’dziko muno (ma passport) zikhala zikutuluka posachedwapa.

A Zikhale Ng’oma ati izi zili chomwechi chifukwa ntchito yosindikiza ma passport inayamba ndipo akuyesetsa kuti idzifulumira.

Iwo amatsimikizira anthu amene anapita ku ofesi za Immigration mu mzinda wa Blantyre, pamene iwo anakayendera malowa.

Pa tsiku, Immigration ikutulutsa ma passport okwana 500, omwe a Ng’oma ati ndi osakwanira.

Olemba: Charles Chindongo
#MBCDigital
#Video

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Asilikali agwira nzika 276 zozembetsedwa zaku Ethiopia

Beatrice Mwape

Govt launches cooperative leadership training

Charles Pensulo

IMMIGRATION DEPORTS 11 FOREIGNERS

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.