Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Boma likuyesetsa kutulutsa ma Passport — Zikhale Ng’oma

Nduna yoona chitetezo cha m’dziko, a Ken Zikhale Ng’oma, yati ziphaso zolowera ndi kutulukira m’dziko muno (ma passport) zikhala zikutuluka posachedwapa.

A Zikhale Ng’oma ati izi zili chomwechi chifukwa ntchito yosindikiza ma passport inayamba ndipo akuyesetsa kuti idzifulumira.

Iwo amatsimikizira anthu amene anapita ku ofesi za Immigration mu mzinda wa Blantyre, pamene iwo anakayendera malowa.

Pa tsiku, Immigration ikutulutsa ma passport okwana 500, omwe a Ng’oma ati ndi osakwanira.

Olemba: Charles Chindongo
#MBCDigital
#Video

Related posts

Tussle for Beach Soccer HTD National Champion

Rabson Kondowe

Msonkho pa ma belo wabwerera kuzakale

Rabson Kondowe

‘Thetsani nkhanza kwa anthu achialubino’

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.