Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Anthu ayamikira ntchito zabwino za Kapusa

Malemu Geoffrey Kapusa waikidwa mmanda lero kumudzi kwawo.

Anthu osiyanasiyana anali nawo pa mwambowu, ndipo onse anati Geoffrey wasiya mbiri yotamandika pankhani zoulutsa mawu pakanema m’dziko muno.

Geofrey “Mr Splash” Kapusa anamwalira dzana pachipatala cha Queen Elizabeth Central mu mzinda wa Blantyre.

Iye anadziwika kwambiri ndikuthandiza oyimba kuti adziwike kudzera mu programme yake ya Music Splash pa kanema ya MBC, kuyambira pomwe inkayamba kumene ngati TVM.

Geoffrey, yemwe anabadwa m’chaka cha 1971, wasiya ana atatu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

WHO warns against falsified medication

MBC Online

Bungwe la MEC lalowa mu mgwirizano obwerekana katundu ndi bungwe la ECZ

MBC Online

Amangidwa poganiziridwa kuti anaba katundu wa ofesi

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.