Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local Local News

ADMARC ayipatsa K 40 Billion yogulira chimanga

Bungwe la Admarc lapatsidwa ndalama zokwana K40 billion kuti liyambenso kugwira ntchito zake modalirika komanso kuyamba kuyendetsa ntchito zake ngati bungwe lochita malonda.

Nduna ya zachuma, a Simplex Chithyola Banda, anena izi pamene akupereka ndondomeko yazachuma ya chaka chaboma cha 2024/2025.

A Banda ati National Food Reserve Agency yapatsidwa K12 billion yogulira chimanga.

Related posts

Chakwera to arrive in BT

Romeo Umali

Arts in the Park unlocks Mw’s potential in the creative sector

Alinafe Mlamba

Malawi Beach Soccer National Team promises fireworks in AFCON Beach Soccer Qualifier

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.