Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Ndege ya Russia ayipeza

Zidutswa za ndege imene inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazhets m’dziko la Russia azipeza.

Malinga ndi unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dzikolo, anthu 17 afa pa ngoziyi ndipo ena asanu sanawapeze.

Ndegeyi inanyamula anthu 22.

Padakali pano, ntchito yoyang’ana anthu amene sanawapeze idakali mkati.

Olemba: Alufisha Fischer

Related posts

Construction of ICT lab excites learners at Chintheche CDSS

Rabson Kondowe

Zomba approves K51.9 Billion 2025/26 Budget

Romeo Umali

‘They believed she was possessed’: Inside Mwanza’s backstreet church that overruled medical care

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.