Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Ndege ya Russia ayipeza

Zidutswa za ndege imene inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazhets m’dziko la Russia azipeza.

Malinga ndi unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dzikolo, anthu 17 afa pa ngoziyi ndipo ena asanu sanawapeze.

Ndegeyi inanyamula anthu 22.

Padakali pano, ntchito yoyang’ana anthu amene sanawapeze idakali mkati.

Olemba: Alufisha Fischer

Related posts

President Chakwera to commemorate Martyrs’ Day in the North

Rabson Kondowe

‘Akabaza kalembetseni m’kaundula wa voti’

Romeo Umali

Chithyola Banda urges banks to lead in financial inclusion

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.