Malawi Broadcasting Corporation
International News Nkhani

Ndege ya Russia ayipeza

Zidutswa za ndege imene inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazhets m’dziko la Russia azipeza.

Malinga ndi unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dzikolo, anthu 17 afa pa ngoziyi ndipo ena asanu sanawapeze.

Ndegeyi inanyamula anthu 22.

Padakali pano, ntchito yoyang’ana anthu amene sanawapeze idakali mkati.

Olemba: Alufisha Fischer

Related posts

Activists denounce continued torture of the elderly

Romeo Umali

Ntchisi District Children’s Parliament launches second session

Romeo Umali

Chileka Police condemns suicide

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.