Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

President Chakwera apitiliza ulendo m’chigawi cha ku m’mawa

Popitiriza ndi ulendo wake m’chigawo chakummawa kwa dziko lino, Prezidenti Dr Lazarus Chakwera lero ayendera chitukuko chosiyanasiyana m’boma la Balaka.

Mtsogoleri wadziko linoyu ayendera Demeter Mega Farm ku Nkaya ndipo kenaka akayendera fakitale yopanga cement ya kampani ya Portland kwa mfumu yayikulu Nsamala ku Balaka komweko.

Kenaka, Dr Chakwera akakhala mlendo olemekezeka pamwambo okondwelera kuti bungwe logawa ngongole la NEEF tsopano lakwanitsa kugawa ngongole zokwana K1 billion.

Mwambowu ukuchitikira pa bwalo la zamasewero la Balaka.

 

Related posts

PRISAM STRIKES PARTNERSHIP TO ENHANCE TEACHER DEVELOPMENT

McDonald Chiwayula

Msika wa fodya ukhoza kudzetsa kukhazikika kwa Kwacha

Rabson Kondowe

RBM Secures World Bank Facility for Manufacturers

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.