Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Bus ya Bullets yachotsedwa ku khothi

Bus ya timu ya FCB Nyasa Big Bullets yachotsedwa kumalo amene amayisunga, ku bwalo la milandu la Blantyre High Court m’mawa uno.

Bus yi inali kumeneku chifukwa cha ngongole imene timuyi idali nayo ndi mphunzitsi wawo wakale, Franco Ndawa, yomwe ayilipira masiku angapo apitawo.

 

Related posts

MCCCI hailed for setting business agenda

Rabson Kondowe

Karonga United wins first home match against Mighty Tigers

Rabson Kondowe

PAC to ‘name and shame’ public officers failing to declare assets

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.