Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Bus ya Bullets yachotsedwa ku khothi

Bus ya timu ya FCB Nyasa Big Bullets yachotsedwa kumalo amene amayisunga, ku bwalo la milandu la Blantyre High Court m’mawa uno.

Bus yi inali kumeneku chifukwa cha ngongole imene timuyi idali nayo ndi mphunzitsi wawo wakale, Franco Ndawa, yomwe ayilipira masiku angapo apitawo.

 

Related posts

President Chakwera wati atsogoleri a mipingo ali ndi ntchito yayikulu

Romeo Umali

RBM launches new payments strategy to drive digital economy

McDonald Chiwayula

Paramount Chief Kyungu urges Malawians to mourn Chilima in peace

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.