Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Bus ya Bullets yachotsedwa ku khothi

Bus ya timu ya FCB Nyasa Big Bullets yachotsedwa kumalo amene amayisunga, ku bwalo la milandu la Blantyre High Court m’mawa uno.

Bus yi inali kumeneku chifukwa cha ngongole imene timuyi idali nayo ndi mphunzitsi wawo wakale, Franco Ndawa, yomwe ayilipira masiku angapo apitawo.

 

Related posts

Athana ndi umphawi pokonza sopo

Romeo Umali

Anthu ena akusowabe pokhala – Paramount Chief Kaduya

Rabson Kondowe

Minibus driver, passengers involved in an accident

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.