Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Bus ya Bullets yachotsedwa ku khothi

Bus ya timu ya FCB Nyasa Big Bullets yachotsedwa kumalo amene amayisunga, ku bwalo la milandu la Blantyre High Court m’mawa uno.

Bus yi inali kumeneku chifukwa cha ngongole imene timuyi idali nayo ndi mphunzitsi wawo wakale, Franco Ndawa, yomwe ayilipira masiku angapo apitawo.

 

Related posts

Biden urges world leaders to join forces in combatting drug trafficking

Mayeso Chikhadzula

Lumbadzi Police engages motorcycle operators to promote road safety

Romeo Umali

Jenda Police arrest suspected murderous duo

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.