Mkulu wa achinyamata m’chipani cha Malawi Congress (MCP) yemwenso ndi nduna ya maboma ang’ono, a Richard Chimwendo Banda, walangiza anthu amdera lakuzambwe m’boma la Mangochi...
President Dr Lazarus Chakwera is this morning witnessing the signing ceremony of the first trilateral partnership between Zambia, Malawi and the North Carolina National Guard,...
Malawi’s effort in promoting the use of clean energy has been energized following a visit by Afrox officials, suppliers of industrial gas. The team visited...
Nduna yoona zamphamvu zamagetsi, a Ibrahim Matola, yomwe imachita nawo msonkhano waukulu wamaiko apa dziko lonse wokambirana zamphamvu zamagetsi wa World Energy Congress ku Rotterdam...
Khothi la Magistrate mu mzinda wa Blantyre la lamula kuti abambo atatu akagwire ukayidi kwa zaka ziwiri komanso chaka ndi theka kaamba kopezeka olakwa pochita...
Bwalo la Milandu la High Court mumzinda wa Lilongwe lathetseratu mlandu wa pakati pa ochita malonda a ku Nsungwi, Area 25 ndi m’mwenye Akbar Salahudding...
Anthu ochita malonda ochokela ku Nsungwi ku Area 25 mu mzinda wa Lilongwe asonkhana panja pa bwalo la High Court kumene akuyembekezera kuti amve chigamulo...
The Ministry of Education has reaffirmed its dedication to advancing inclusive education in line with Malawi 2063 objectives. Line minister, Madalitso Kambauwa Wirima, emphasised this...
Yemwe anaakhalapo mkulu wa nthambi ya CID, a George Mnjale, amwalira lero ku chipatala cha Kamuzu Central mumzinda wa Lilongwe kumene amalandira thandizo. A Mnjale...
The Secretary to the President and Cabinet, Colleen Zamba, says Principal Secretaries in Ministries are crucial in formulating and implementing the government’s policies. Zamba was...