Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Tidzagwira ntchito mwaukadaulo pa chisankho cha 2025, watero mkulu wa MBC

Mkulu wa bungwe lowulutsa mawu la Malawi Broadcasting Corporation (MBC), a George Kasakula, ati bungwe lawo lidzagwira ntchito mwaukadaulo ndi mopanda kukondera pa chisankho cha chaka cha mawa.

A Kasakula anena zimenezi ku Lilongwe pa zokambirana zokhudza ndondomeko zomwe bungwe la MBC lakonza zothandiza kuti lidzatumikire aMalawi popanda vuto.

Pa msonkhanowu pali alembi a zipani zosiyanasiyana monga MCP, DPP, UDF, Aford ndi zina zambiri komanso wapampando wa bungwe la atolankhani la Misa.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

‘Boma likukumana ndi zovuta polimbana ndi mchitidwe wa nkhanza kwa anthu achikulire’

Beatrice Mwape

Akhazikitsa chipani chatsopano

MBC Online

Ana 169 apulumutsidwa ku maukwati

Lonjezo Msodoka
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.