Author : Blessings Kanache
Media Council drills journalists on safety during elections
The Media Council of Malawi (MCM) has urged journalists to prioritise their safety when covering elections. MCM Executive Director Moses Kaufa made the remarks during...
‘Osazembetsa thandizo la chimanga’
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi wati ndi okhumudwa ndi mchitidwe wa anthu ena amene akumaba thandizo la chimanga lomwe Boma likupereka...
ACB urged to conclude corruption cases
Minister of Information and Digitalisation, Moses Kunkuyu, has urged the Anti Corruption Bureau (ACB) to handle corruption cases quickly to instil confidence in Malawians in...
Inclusive social protection crucial for persons with disabilities
Government says the new national social protection policy will help foster the inclusiveness of persons with disabilities. Ben M’bwana, Director of Administration in the Ministry...
Kulowetsa galimoto mozemba ndi mlandu
Bungwe lotolera misonkho la Malawi Revenue Authority MRA lati likukumana ndi mavuto pa ntchito yotolera misonkho, maka pa galimoto zimene zimalowa m’dziko muno mozemba. Mkulu...
Tikuyesetsa kuti magetsi ayake mwachangu, ESCOM yatero
Bungwe la ESCOM lati makina ake a magetsi anadzithimitsa lero nthawi itatsala mphindi 18 kuti ikwane 12 koloko masana. Malinga ndi chikalata chomwe a ESCOM...
Kampani yatsopano ya magetsi adzuwa ikubwera
Kampani ya ku Germany yopanga magetsi a dzuwa ya Sun Power Africa Development yasainira mgwirizano ndi boma la Malawi odzayambitsa ntchito yopanga magetsi okwana 50...
Mgwirizano wamaulendo apa madzi watheka
Dziko la Malawi lasayinira mgwirizano ndi kampani zomwe zimapanga komanso kuyendetsa ntchito za sitima za pamadzi kuti zidzayambitse ntchitoyi pa nyanja ya Malawi. Mtsogoleri wa...