Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Chakwera ayendera chitukuko cha mphepete mwa nyanja ku Mangochi

Mtsogoleri wadziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akuyendera ntchito zosiyanasiyana zachitukuko m’boma la Mangochi.

Kuchoka apo, Dr Chakwera ayendera ntchito yomanga ofesi yatsopano ku khonsolo ya Mangochi, ntchito yomwe boma likugwira mogwirizana ndi dziko la Iceland.

Kenako, Dr Chakwera afika ku Monkey Bay, kumene ayenderenso ntchito ya msewu wa Monkey Bay – Cape Maclear- T378 mdera la mfumu yaikulu Nankumba.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Standard Bank gives K25 million towards 2024 Mother’s Fun Run

Romeo Umali

DC advises social cash transfer beneficiaries to buy maize

Romeo Umali

FAM hands 100 footballs to SULOM

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.