Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Chakwera ayendera chitukuko cha mphepete mwa nyanja ku Mangochi

Mtsogoleri wadziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akuyendera ntchito zosiyanasiyana zachitukuko m’boma la Mangochi.

Kuchoka apo, Dr Chakwera ayendera ntchito yomanga ofesi yatsopano ku khonsolo ya Mangochi, ntchito yomwe boma likugwira mogwirizana ndi dziko la Iceland.

Kenako, Dr Chakwera afika ku Monkey Bay, kumene ayenderenso ntchito ya msewu wa Monkey Bay – Cape Maclear- T378 mdera la mfumu yaikulu Nankumba.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

SADC Calls for fresh elections in Madagascar

Romeo Umali

Four Young Scorchers given chance at senior level

Romeo Umali

Experts warn of rising eye problems amid unsafe treatments

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.