Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Dr Chakwera ayendera chitukuko cha mphepete mwa nyanja ku Mangochi

Mtsogoleri wadziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akuyendera ntchito zosiyanasiyana zachitukuko m’boma la Mangochi.

Kuchoka apo, Dr Chakwera ayendera ntchito yomanga ofesi yatsopano ku khonsolo ya Mangochi, ntchito yomwe boma likugwira mogwirizana ndi dziko la Iceland.

Kenako, Dr Chakwera afika ku Monkey Bay, kumene ayenderenso ntchito ya msewu wa Monkey Bay – Cape Maclear- T378 mdera la mfumu yaikulu Nankumba.

Olemba: Owen Mavula

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

WOMAN JAILED 5 YEARS FOR WOUNDING STEPDAUGHTER

MBC Online

Maso Awards eyes international platform

Romeo Umali

CHAKWERA INSPIRES HOPE AGAINST  HUNGER

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.