Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Young Stunna wafafaniza machimo ku Blantyre

Anthu amunzinda wa Blantyre anali okondwa kwambiri ataonelera maimbidwe ochititsa chidwi kuchoka kwa oimba wa chamba cha amapiano, Young Stunna, wochokera m’dziko la South Africa.

Mwambowu unali wachiwiri a Beerland and Classic Events atawukonzanso Young stunna atalephera kubwera m’mwezi wa May chaka chino.

Ena omwe anaimbanso kumwambowu anali Kell Kay, Eli Njuchi, Zeze Kingston, Tuno komanso Fada Moti.

Olemba: Andrew Lambulira

Related posts

Mchinji Villa, CIVO in FDH quarters

Romeo Umali

Nomads unbeaten as TNM Super League hits Mid-Season mark

Romeo Umali

CHAKWERA HOMECOMING MONDAY

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.