Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Local Local Music News Nkhani

Muzilimbikira ngakhale mutakumana ndi mavuto — Sife

Oyimba Silvia ‘Sife’ Sande, amene amadziwika bwino ndi nyimbo yake yotchedwa Kumaloto, walimbikitsa anthu m’dziko muno kuti ngakhale atakumana ndi mavuto adzingolimbikira ndipo asamadziyerekeze ndi ena.

Iye wati anthu ambiri amene amaoneka ngati opanda mavuto nawonso amakhala akukumana ndi mikwingwirima yosiyanasiyana.

Chifukwa cha ichi, Sife wayimba nyimbo yatsopano yotchedwa ‘Amafukeni’ pamodzi ndi K Banton komanso Jolasto ndipo ndi yolimbikitsa anthu.

Katswiri oyimbayu anapemphanso anthu kuti asamaganize zochotsa moyo wawo chifukwa nyengo iliyonse imakhala ndi pothera pake.

Related posts

Karonga District Council cracks whip on uncomplying mill operators

Romeo Umali

Opposition parties afraid of elections – Umodzi Party

Rabson Kondowe

Chakwera deserves second term – MCP diaspora wing

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.