Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

‘Tikufufuza’

Boma, kudzera ku unduna oona za maubale a dziko lino ndi maiko akunja, lati likufufuzabe malipoti akuti aMalawi ena amwalira pa ngozi ya nyumba yosanjikana imene yagwa m’dziko la South Africa.

Ofalitsankhani ku undunawu, a Charles Nkhalamba, ati akuchita kafukufuku kudzera ku ofesi ya kazembe wa dziko lino ku South Africako.

Nyumbayi idagwa m’dera la George ndi kupha anthu asanu ndi atatu. Anthu 81 ndi amene akuganiziridwa kuti anali pamalopo.

 

Related posts

Nearly 70 percent of children in Malawi multi-dimensionally poor – Report

Alinafe Mlamba

PRISAM IMPRESSED WITH MSCE PROGRESS

McDonald Chiwayula

Carbon credit hidden treasure for Malawi – financial expert

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.