Malawi Broadcasting Corporation
Local News

Tigwire ntchito limodzi – Kamtukule

Nduna ya zokopa alendo, a Vera Kamtukule, yalimbikitsa anthu m’dziko muno kuti adzigwira ntchito limodzi ndi akatswiri a zachilengedwe pa ntchito yobzyala mitengo.

A Kamtukule ati izi ndi zofunika kaamba kakuti mitengo imafunika chisamaliro ikamakula, potwngeranso kuti anthu amadzala mitengo 10 million pa chaka koma 100,000 yokha ndiyo imakula.

Izi zinadziwika pa ntchito yobzyala mitengo kudera la mfumu yayikulu Maganga m’boma la Salima.

Related posts

Student hopes to excel in English at regional Spelling Bee contest

Romeo Umali

World Bank lauds Chikwawa District Council

Romeo Umali

Bullets sign Chitiyo

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.