Malawi Broadcasting Corporation
Local News

Tigwire ntchito limodzi – Kamtukule

Nduna ya zokopa alendo, a Vera Kamtukule, yalimbikitsa anthu m’dziko muno kuti adzigwira ntchito limodzi ndi akatswiri a zachilengedwe pa ntchito yobzyala mitengo.

A Kamtukule ati izi ndi zofunika kaamba kakuti mitengo imafunika chisamaliro ikamakula, potwngeranso kuti anthu amadzala mitengo 10 million pa chaka koma 100,000 yokha ndiyo imakula.

Izi zinadziwika pa ntchito yobzyala mitengo kudera la mfumu yayikulu Maganga m’boma la Salima.

Related posts

Natural Resources Ministry needs K1.2 billion

Romeo Umali

ADL to construct Airport City

Romeo Umali

Karonga United triumph over Baka City

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.