Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Prezidenti Chakwera ndi wa masomphenya — Mkaka

A Eisenhower Mkaka omwe ndi mlembi wamkulu wa chipani cha MCP ayamikila m’tsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera kaamba kopititsa patsogolo ndale za demokalase.

A Mkaka ati Dr Chakwera amasankha anthu m’maudindo potengela nzeru zao osati ndale ndipo ati izi zili chomwechi kutsatira pamene anthu ambiri ochoka m’zipani zina akulowa chipani cha Kongolesi chifukwa iwo akuchita zakupsya posintha dziko lino pa chitukuko.

Iwo ayamikanso ntchito yaikulu yomwe alimi akugwira m’dziko muno pothandizila kuti m’dziko muno mudzipezeka ndalama za kunja.

Related posts

Chitaninso ulimi wa ziweto — NEEF

Romeo Umali

Boma ligula PREP ochuluka chaka chamawa

Rabson Kondowe

‘Ntchito yomanga misewu ikuyenda bwino ku Lilongwe’

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.