Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Prezidenti Chakwera ndi wa masomphenya — Mkaka

A Eisenhower Mkaka omwe ndi mlembi wamkulu wa chipani cha MCP ayamikila m’tsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera kaamba kopititsa patsogolo ndale za demokalase.

A Mkaka ati Dr Chakwera amasankha anthu m’maudindo potengela nzeru zao osati ndale ndipo ati izi zili chomwechi kutsatira pamene anthu ambiri ochoka m’zipani zina akulowa chipani cha Kongolesi chifukwa iwo akuchita zakupsya posintha dziko lino pa chitukuko.

Iwo ayamikanso ntchito yaikulu yomwe alimi akugwira m’dziko muno pothandizila kuti m’dziko muno mudzipezeka ndalama za kunja.

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

‘Tidziyamba ndife aMalawi kutsatsa malonda a dziko lathu’

McDonald Chiwayula

Nyimboyi ithandize onse osweka mitima – Sife Mw

Emmanuel Chikonso

Wapereka mbatata yophika kuti asamuulure kuti wagwilira ana awiri

Charles Pensulo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.