Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Tourism

President Chakwera ayendera ntchito zachitukuko ku Mangochi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno ali pa ulendo oyendera ntchito zachitukuko m’boma la Mangochi.

Dr Chakwera akuyembekezeka kuyendera komanso kucheza ndi anthu ogwira ntchito zokopa alendo ndipo ena mwa malowa ndi a Rosalyn’s Beach Hotel.

Dr Chakwera ayenderanso kampani yopanga cement ya Cement Products Limited ku Njereza ndipo akatero akayendera malo antchito zokopa alendo a Club Makokola komwenso akacheze ndi ogwira ntchito zamalonda.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Waluso asamatuwe ndi umphawi — Wendy

Romeo Umali

MRCS yagawa K180 million m’boma la Karonga

Romeo Umali

Become job creators, not seekers — Kabwira

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.