Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Tourism

President Chakwera ayendera ntchito zachitukuko ku Mangochi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno ali pa ulendo oyendera ntchito zachitukuko m’boma la Mangochi.

Dr Chakwera akuyembekezeka kuyendera komanso kucheza ndi anthu ogwira ntchito zokopa alendo ndipo ena mwa malowa ndi a Rosalyn’s Beach Hotel.

Dr Chakwera ayenderanso kampani yopanga cement ya Cement Products Limited ku Njereza ndipo akatero akayendera malo antchito zokopa alendo a Club Makokola komwenso akacheze ndi ogwira ntchito zamalonda.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

MCHA warns students of scammers

Rabson Kondowe

PMI, MNCS partner ahead of Blantyre race

Rabson Kondowe

Nsanje police launches man-hunt for assailants

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.