Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Tourism

President Chakwera ayendera ntchito zachitukuko ku Mangochi

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno ali pa ulendo oyendera ntchito zachitukuko m’boma la Mangochi.

Dr Chakwera akuyembekezeka kuyendera komanso kucheza ndi anthu ogwira ntchito zokopa alendo ndipo ena mwa malowa ndi a Rosalyn’s Beach Hotel.

Dr Chakwera ayenderanso kampani yopanga cement ya Cement Products Limited ku Njereza ndipo akatero akayendera malo antchito zokopa alendo a Club Makokola komwenso akacheze ndi ogwira ntchito zamalonda.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Kasambara laid to rest

Rabson Kondowe

LCC urges contractors to produce standard work

Romeo Umali

Human First reaches out to 17 million people 30 years

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.