Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Ofesi ya khonsolo ya Mangochi yatsopano idzathandiza koposa’

Ntchito yomanga ofesi ya tsopano ya khonsolo ya Mangochi akuti ithandiza kwambiri m’mene adindo amagwilira ntchito.

Izi zili chomwechi kaamba koti adindo anthambi zambiri zofunikira adzigwira ntchito pamalo amodzi kusiyana ndi mmene zinthu zilili pano pamene ofesi zili mbali ina ya town ya Mangochi.

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, masanawa anayendera ntchito yomanga ofesiyi ndipo anabzyalapo mtengo.

Pakadali pano, Dr Chakwera ndi Mayi Monica Chakwera anyamuka ulendo opita kukayendera ntchito yomanga msewu wa Monkey Bay – Cape Maclear.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

World Bank tips Malawi on economic recovery

Rabson Kondowe

Achewa athira nsembe

Romeo Umali

PLMB injects K3.5 million towards Phiri’s bout

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.