Malawi Broadcasting Corporation
International News

Ntchito yofufuza ndege m’dziko la Russia yayamba

Akuluakulu a unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dziko la Russia ati ndege ya mtundu wa MI-8T inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazlets ndipo inaynamula anthu okwana 22.

Unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidziwu wati chifunga ndi chomwe chikuchitisa kuti ntchito yosaka ndegeyi ikhale yovuta

By Alufisha Fischer

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Journalists urged to invest in assets

Simeon Boyce

Wanderers secure second place

Romeo Umali

Chakwera tours Tropha Estates

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.