Malawi Broadcasting Corporation
International News

Ntchito yofufuza ndege m’dziko la Russia yayamba

Akuluakulu a unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidzi m’dziko la Russia ati ndege ya mtundu wa MI-8T inasowa itangonyamuka kumene pa bwalo la ndege la Vachkazlets ndipo inaynamula anthu okwana 22.

Unduna owona za ngozi zogwa mwadzidzidziwu wati chifunga ndi chomwe chikuchitisa kuti ntchito yosaka ndegeyi ikhale yovuta

By Alufisha Fischer

Related posts

ESCOM’s vandalism fight boosted: President assents to the Electricity (Amendment) Act

MBC Online

Do not sell maize – JB

Rabson Kondowe

SDA’s South Malawi Conference launches ministry in higher learning institutions

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.