Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Ndatula pansi udindo wa utsogoleri wa aphungu otsutsa boma — Nankhumwa

Yemwe anali mtsogoleri wa aphungu otsutsa boma ku nyumba ya malamulo, Kondwani Nankhumwa, walengeza kuti watula pansi udindowu.

Iwo ati zikhala zovuta kupitilirabe kukhala pa udindowu pambuyo poyambitsa chipani chawo chatsopano.

Poyankhula munzinda wa Blantyre, iwo ati pakali pano awuza kale owaimira pa mlandu okhudza ofesiyi omwe uli ku bwalo lamilandu kuti awuyimitse.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

NEEF yakhazikitsa ngongole ya ulimi wa mthilira

Mayeso Chikhadzula

Mnyamata wamangidwa atabaya bwenzi lake

Romeo Umali

Boma la Balaka aliyamikira polimbikitsa ntchito za umoyo

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.