Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Ndatula pansi udindo wa utsogoleri wa aphungu otsutsa boma — Nankhumwa

Yemwe anali mtsogoleri wa aphungu otsutsa boma ku nyumba ya malamulo, Kondwani Nankhumwa, walengeza kuti watula pansi udindowu.

Iwo ati zikhala zovuta kupitilirabe kukhala pa udindowu pambuyo poyambitsa chipani chawo chatsopano.

Poyankhula munzinda wa Blantyre, iwo ati pakali pano awuza kale owaimira pa mlandu okhudza ofesiyi omwe uli ku bwalo lamilandu kuti awuyimitse.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

Onesimus achenjeza akonzi a Ku Mingoli Bash

Rabson Kondowe

Atsiriza kufufuza za imfa ya anthu asanu ku Blantyre

Blessings Kanache

Mavuto ndiwo akulimbikitsa mchitidwe odzipha- Chiluzi

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.