Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Politics

“Ndabwela kudzagwira ntchito” — Uladi Mussa

Yemwe anali wachiwiri kwa prezidenti wachipani cha Democratic Progressive Party (DPP), a Uladi Mussa, wati agwira ntchito limodzi ndi atsogoleli achipani cha MCP pofuna kuonetsetsa kuti chipanichi chipitilire kukhala champhamvu.

A Mussa amayankhula ku Dedza pabwalo la Phillip Holseman kumene mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera amachititsa msonkhano wa chitukuko.

Mwa zina a Mussa ati ma area omwe adawakhazikitsa okwana 188 tsopano awasandutsa kukhala a chipani cha MCP.

Iwo adalowa m’chipani cha MCP masiku apitawa kuchoka kuchipani cha DPP ati poona mfundo zabwino zomwe mtsogoleri wa dziko lino akutsatila potsogolela dziko lino.

 

Related posts

Russia reaffirms commitment to Africa’s development through strategic partnerships

Yamikani Simtowe

EMPLOYMENT OPPORTUNITY

MBC Online

Oxfam urges govt to expediate maize imports

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.