Malawi Broadcasting Corporation
Africa Crime Local Local News Nkhani Politics

“Osanyoza anthu achikulire” — Chakwera

President Lazarus Chakwera wati khalidwe lonyoza anthu achikulire powanena kuti ndi mfiti ndi kuwapha (mob justice) zili ndi kuthekera kosokoneza ana achichepere m’dziko muno.

A Chakwera ati ndi pofunikanso kukhala ogwirizana, posatengera kusiyana zipani, zipembedzo ndi zina zambiri popeza anthu akakhala ogwirizana, dziko lino likhoza kupambana nkhondo yolimbana ndi njala.

#ChakweraDevelopmentalRally

Related posts

Malawi to have National Communication policy

Rabson Kondowe

CSOs FOR SANITY

MBC Online

Serve Malawians, Chakwera advises Mumba

Chisomo Manda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.