Malawi Broadcasting Corporation
Africa Crime Local Local News Nkhani Politics

“Osanyoza anthu achikulire” — Chakwera

President Lazarus Chakwera wati khalidwe lonyoza anthu achikulire powanena kuti ndi mfiti ndi kuwapha (mob justice) zili ndi kuthekera kosokoneza ana achichepere m’dziko muno.

A Chakwera ati ndi pofunikanso kukhala ogwirizana, posatengera kusiyana zipani, zipembedzo ndi zina zambiri popeza anthu akakhala ogwirizana, dziko lino likhoza kupambana nkhondo yolimbana ndi njala.

#ChakweraDevelopmentalRally

Related posts

Makina othandiza vuto la impso akonzedwa ku QECH

Romeo Umali

Apolisi ku Mangochi amanga Boika atam’peza ndi chida choopsya

Romeo Umali

BRAZILIAN SPECIALIST PLEDGES CATARACT SURGERY FOR 1000 MALAWIANS

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.