Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Msika wa fodya wayamba bwino ku Limbe

Alimi a fodya m’dziko muno ati ndiosangalala ndi m’mene malonda a fodya ayambira pa msika.

President wa Tobacco Association of Malawi (TAMA) trust, a Abiel Kalima Banda, ati mitengo ya fodya ya chaka chino yaposa zaka zam’mbuyomu.

“Mitengo imeneyi ilimbikitsa alimi pa ulimi wawo,” atero a Kalima Banda.

Malonda a fodya ku Limbe ayamba pa mtengo wa  3 dollars 11 cents ndipo mtengo otsika ndi 2 dollars 20 cents.

Related posts

Run with vision, Chakwera tells clergy

Romeo Umali

Suspected armed robber faces murder charges

Rabson Kondowe

A better Malawi is possible – Chithyola Banda

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.