Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Kawale akuyendela ntchito ya Shire Valley Transformation

Nduna ya zaulimi a Sam Kawale lero ikuyendela ntchito yomanaga ngalande yodutsa madzi aulimi wanthilira pansi pa Shire Valley Transformation Program mboma la Chikwawa.

Ndunayi ayifotokozela kusintha komwe kulipo pama plan omanga ngalandeyi kamba ka Namondwe Ana yemwe anakokolola zomangamanga zina za ntchito yi mchaka cha 2022.

Gawo loyamba lomanga ngalandeyi ifika kumapeto mkatikati mwa chaka cha mawa.

 

Olemba Chipiliro Mtumodzi

Related posts

Flames imenya World Cup boma likathandiza moyenera — Haiya

Romeo Umali

Learner mentors making a difference in Mchinji Schools

Romeo Umali

Chichiri Court gets digital upgrade

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.