Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Kale Langa yagwedeza Kaning’ina

Gulu lovina dansi pa pologalamu yapa wailesi ya Kale Langa imene imauluka pa MBC Radio one yasonkhana mu mzinda wa Mzuzu kumene akuvina dansiyo.

Mkonzi komanso muulutsi wa Pologalamuyo Sol Rasheed wati ndi okondwa kuti wachititsa Pologalamuyo live mu Mzinda wa Mzuzu kumenenso akuti wakumana ndi anthu amene amangowamva akamalemba kalata zawo pa Wailesi.

Anthuwo asangalala ndi Nyimbo za Simanjemanje komanso Kanindo zimene awonetsa luso lawo mmene amkachitira kalero popalasa fumbi mu dansi yobetcha imene amkavina mu nthawi yawo.

Wolemba: Hassan Phiri

Related posts

Bushiri agawa chakudya kwa okhudzidwa ndi njala ku Nkhotakota

Yamikani Simtowe

Blue Eagles yatsala ndi ma poyinsi atatu kuti ibwerere mu super league

Rabson Kondowe

Pasuwa akukhulupilira kuti Bullets iyambaso kuchita bwino

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.