Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Giboh Pearson wapulumuka ku ngozi

Katswiri oyimba amene amachokera m’boma la Phalombe, Giboh Pearson, wapulumuka pa ngozi ya galimoto yomwe wachita pomwe amapita ku phwando la msangulutso ku Bangwe mu mzinda wa Blantyre.

Malinga ndi Pearson, chiwongolero komanso mabuleki agalimoto lake zinasiya kugwira ntchito, zomwe zinachititsa kuti akanike kuwongolera galimotoli ndipo linatembenuzika.

“Ndachita ngozi koma ndili bwino,” watero Giboh patsamba lake la mchezo.

Pangoziyi palibe wavulala.

 

Related posts

Chakwera dates journalists

Gawo lachitatu la kalembera wazisankho wayamba

Romeo Umali

Mwambo wamapemphero uli mkati ku nyumba ya chisoni

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.