Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Giboh Pearson wapulumuka ku ngozi

Katswiri oyimba amene amachokera m’boma la Phalombe, Giboh Pearson, wapulumuka pa ngozi ya galimoto yomwe wachita pomwe amapita ku phwando la msangulutso ku Bangwe mu mzinda wa Blantyre.

Malinga ndi Pearson, chiwongolero komanso mabuleki agalimoto lake zinasiya kugwira ntchito, zomwe zinachititsa kuti akanike kuwongolera galimotoli ndipo linatembenuzika.

“Ndachita ngozi koma ndili bwino,” watero Giboh patsamba lake la mchezo.

Pangoziyi palibe wavulala.

 

Related posts

Admarc idzigula chimanga pamtengo okwera

Romeo Umali

CHAKWERA ATTENDS COMMONWEALTH LEADERS MEETING

MBC Online

‘Boma ligwirane manja ndi opanga fetereza wa Mbeya’

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.