Malawi Broadcasting Corporation
Development Local News Nkhani Sports Sports

Dedza Dynamos yatola chikwama

Timu ya Dedza Dynamos tsopano izidziwika kuti Premeir Bet Dedza Dynamos kutsatira m’gwirizano umene yakhazikitsa ndi kampani ya Premier Bet wa ndalama zokwana K100 million wa chaka chimodzi.

Ngati mbali imodzi yowalimbikitsa osewera a timuyi, Premier Bet idzipereka ndalama zokwana K100,000 kwa osewera bwino pa mwezi ndipo K500,000 idzipita kwa osewera bwino pa chaka.

Otsatira komanso kuchemelera timuyi ndi amene adzisankha osewerawa ndipo ndalama yokwana K200,000 idzipita kwa ochemelera amene waonetsa chikondi ku timuyi.

Olemba : Amin Mussa

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Child injured as bus shelter collapses in Mangochi

MBC Online

MUBAS champions research and innovation for Malawi 2063

MBC Online

Parliament to meet late August

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.