Malawi Broadcasting Corporation
Development Local News Nkhani Sports Sports

Dedza Dynamos yatola chikwama

Timu ya Dedza Dynamos tsopano izidziwika kuti Premeir Bet Dedza Dynamos kutsatira m’gwirizano umene yakhazikitsa ndi kampani ya Premier Bet wa ndalama zokwana K100 million wa chaka chimodzi.

Ngati mbali imodzi yowalimbikitsa osewera a timuyi, Premier Bet idzipereka ndalama zokwana K100,000 kwa osewera bwino pa mwezi ndipo K500,000 idzipita kwa osewera bwino pa chaka.

Otsatira komanso kuchemelera timuyi ndi amene adzisankha osewerawa ndipo ndalama yokwana K200,000 idzipita kwa ochemelera amene waonetsa chikondi ku timuyi.

Olemba : Amin Mussa

Related posts

DODMA secures 6000 metric tons of Maize

Alinafe Mlamba

New Puma MD determined to make gas cheaper

Romeo Umali

Low turnout for voter registration in Mchinji

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.