Malawi Broadcasting Corporation
Africa Entertainment Local Local Music News

BWANJI SIMUNANENE?

Oyimba Nyimbo za Uzimu Evance Meleka, watulutsa nyimbo imene ikukhuza imfa ya oyimba odziwika bwino Katelele Ching’oma.
Nyimbo-yi yomwe ikudziwika kuti “Bwanji Simunanene?” Muli uthenga odandaula za kumwalira kwa oyimba ena monga Atoth Manje ndi Thomas Chibade.
Ching’oma wamwalira dzulo ku chipatala cha Kamuzu Central mu mzinda wa Lilongwe atangodwala kwa nthawi yochepa.
Pangodutsa miyezi Iwiri ndi sabata ziwiri zokha pamene oyimba onsewa atsikira kuli chete.
Olemba : Romeo Umali.
Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Nurses are backbone of health care delivery – NONM

MBC Online

Anglican Women urged to protect girls’ health

Arthur Chokhotho

Beach Soccer can transform players’ lives — Chimbalanga

Rudovicko Nyirenda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.