Malawi Broadcasting Corporation
Africa Entertainment Local Local Music News

BWANJI SIMUNANENE?

Oyimba Nyimbo za Uzimu Evance Meleka, watulutsa nyimbo imene ikukhuza imfa ya oyimba odziwika bwino Katelele Ching’oma.
Nyimbo-yi yomwe ikudziwika kuti “Bwanji Simunanene?” Muli uthenga odandaula za kumwalira kwa oyimba ena monga Atoth Manje ndi Thomas Chibade.
Ching’oma wamwalira dzulo ku chipatala cha Kamuzu Central mu mzinda wa Lilongwe atangodwala kwa nthawi yochepa.
Pangodutsa miyezi Iwiri ndi sabata ziwiri zokha pamene oyimba onsewa atsikira kuli chete.
Olemba : Romeo Umali.

Related posts

How APM solved food puzzle in first 100 days

MBC Online

Churches urged to champion ARV uptake

Alinafe Mlamba

Two brothers nabbed over possessing Cannabis without permit

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.