Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Ayamba kumanga anthu ogulitsa “ambuye tengeni”

Apolisi mchigawo chakummwera ati tsopano ayamba kumanga anthu onse omwe akugulitsa mowa owopsa wa ‘ambuye tengeni’ omwe waphetsa anthu asanu kwa Manase ku Blantyre.

Anthu ena atatu ali m’chipatala.

Mneneri wa a polisi mchigawochi, a Joseph Sauka, ati apolisi ali kale mmadera osiyanasiyana komwenso akulanda mowawu, omwe ati ndi owopsa kwambiri.

“Cholinga chathu ndikuteteza anthu ku imfa zodza kamba kakumwa mowa osavomerezeka, omwenso ndi owopsa,” atero a Sauka.

Related posts

Kampani zamigodi ziyike umwini pa MSE — Misalico

Romeo Umali

Boma sililekelera chinyengo — Usi

Rabson Kondowe

Drones key in disaster response – African Drone and Data Academy

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.