Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Anamalira akhamukira ku CI

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi katswiri pa zamalamulo Ralph Kasambara wayamba ku CI mu mzinda wa Blantyre.

Akuluakulu osiyanasiyana kuphatikizapo a boma, a zipani za ndale komanso mipingo, ali nawo pa mwambowu.

Thupi la a Kasambara ayenda nalo pa ndege kupita ku NkhataBay masana ano ukangotha mwambowu.

 

Related posts

BetWay, Silver Strikers partnership boosts morale

Romeo Umali

Tifalitse uthenga wa matenda a TB ndi Khate — Madam Chakwera

Romeo Umali

Government conducts outreach initiative at KCH

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.