Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Tikuyesetsa kuti magetsi ayake mwachangu, ESCOM yatero

Bungwe la ESCOM lati makina ake a magetsi anadzithimitsa lero nthawi itatsala mphindi 18 kuti ikwane 12 koloko masana.

Malinga ndi chikalata chomwe a ESCOM atulutsa, pakadali pano iwo akuyesetsa kubwezeretsa magetsi m’madera ambiri ngakhale m’madera ena magetsi sanayakebe.

Iwo ati pomwe akufufuza kuti apeze chomwe chinachititsa kuti magetsi azime, akuyesetsanso kubwezeretsa komwe sanayambe kuyaka.

 

Related posts

Tigwirane manja potolera ndalama zoyendetsera ligi — SULOM

Romeo Umali

Bwalo lamasewero la BAT muzidzalowa anthu 17, 000

Romeo Umali

Duo arrested for betting shop theft

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.