Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Tikuyesetsa kuti magetsi ayake mwachangu, ESCOM yatero

Bungwe la ESCOM lati makina ake a magetsi anadzithimitsa lero nthawi itatsala mphindi 18 kuti ikwane 12 koloko masana.

Malinga ndi chikalata chomwe a ESCOM atulutsa, pakadali pano iwo akuyesetsa kubwezeretsa magetsi m’madera ambiri ngakhale m’madera ena magetsi sanayakebe.

Iwo ati pomwe akufufuza kuti apeze chomwe chinachititsa kuti magetsi azime, akuyesetsanso kubwezeretsa komwe sanayambe kuyaka.

 

Related posts

Chakwera Moves in to Find Solution to Street Vending

Alick Sambo

MPICO profit jumps 59% to K19.3bn

McDonald Chiwayula

Minister condemns vandalism of school property

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.