Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Tikuyesetsa kuti magetsi ayake mwachangu, ESCOM yatero

Bungwe la ESCOM lati makina ake a magetsi anadzithimitsa lero nthawi itatsala mphindi 18 kuti ikwane 12 koloko masana.

Malinga ndi chikalata chomwe a ESCOM atulutsa, pakadali pano iwo akuyesetsa kubwezeretsa magetsi m’madera ambiri ngakhale m’madera ena magetsi sanayakebe.

Iwo ati pomwe akufufuza kuti apeze chomwe chinachititsa kuti magetsi azime, akuyesetsanso kubwezeretsa komwe sanayambe kuyaka.

 

Related posts

CSO to lobby for funding for Salima Sugar Company’s expansion

Rabson Kondowe

Multichoice Malawi unveils festive season channel

McDonald Chiwayula

CS-EPWP hailed for cushioning communities from hunger

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.