Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Boma likuyesetsa kutulutsa ma Passport — Zikhale Ng’oma

Nduna yoona chitetezo cha m’dziko, a Ken Zikhale Ng’oma, yati ziphaso zolowera ndi kutulukira m’dziko muno (ma passport) zikhala zikutuluka posachedwapa.

A Zikhale Ng’oma ati izi zili chomwechi chifukwa ntchito yosindikiza ma passport inayamba ndipo akuyesetsa kuti idzifulumira.

Iwo amatsimikizira anthu amene anapita ku ofesi za Immigration mu mzinda wa Blantyre, pamene iwo anakayendera malowa.

Pa tsiku, Immigration ikutulutsa ma passport okwana 500, omwe a Ng’oma ati ndi osakwanira.

Olemba: Charles Chindongo
#MBCDigital
#Video

Related posts

Three Wanderers players nominated for Castel Award

Romeo Umali

Constituents make unrealistic demands — MPs

Yamikani Simtowe

Mussa Ajibu asambitsa chokweza Vissah

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.