Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Ayamba kumanga anthu ogulitsa “ambuye tengeni”

Apolisi mchigawo chakummwera ati tsopano ayamba kumanga anthu onse omwe akugulitsa mowa owopsa wa ‘ambuye tengeni’ omwe waphetsa anthu asanu kwa Manase ku Blantyre.

Anthu ena atatu ali m’chipatala.

Mneneri wa a polisi mchigawochi, a Joseph Sauka, ati apolisi ali kale mmadera osiyanasiyana komwenso akulanda mowawu, omwe ati ndi owopsa kwambiri.

“Cholinga chathu ndikuteteza anthu ku imfa zodza kamba kakumwa mowa osavomerezeka, omwenso ndi owopsa,” atero a Sauka.

Related posts

Apolisi agwira akuba amenenso anagwililira ophunzira ku Domasi Institute College

Romeo Umali

CHAKWERA TO ADDRESS UNGA TODAY

MBC Online

Thyolo ramps up efforts to bolster Covid-19 Vaccine uptake

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.