Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Unduna wa za ulimu watulutsa mitengo ya mbewu

Unduna wa za ulimi watulutsa mitengo yogulira mbewu chaka chino.

Malinga undunawu, chimanga chidzigulidwa pa mtengo osachepera K650, soya K800, thonje K900, nyemba zosasakanikirana K1200, nyemba zosakanikirana K900.

A Sam Kawale, omwe ndi nduna ya za ulimi, adalemba pa tsamba la m’chezo kuti mitengoyi ayikhazikitsa pambuyo pa zokambirana ndi mabungwe osiyanasiyana.

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

Likoma District Council budget now at K3.9 billion

Romeo Umali

Race to September: Parties intensify nationwide rallies

Romeo Umali

Rumphi Police nabs man over suspected murder

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.