Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Unduna wa za ulimu watulutsa mitengo ya mbewu

Unduna wa za ulimi watulutsa mitengo yogulira mbewu chaka chino.

Malinga undunawu, chimanga chidzigulidwa pa mtengo osachepera K650, soya K800, thonje K900, nyemba zosasakanikirana K1200, nyemba zosakanikirana K900.

A Sam Kawale, omwe ndi nduna ya za ulimi, adalemba pa tsamba la m’chezo kuti mitengoyi ayikhazikitsa pambuyo pa zokambirana ndi mabungwe osiyanasiyana.

#MBCDigital
#Manthu

Related posts

All set for Top Product Awards 2024

McDonald Chiwayula

Chakwera to attend 79th UNGA session

Romeo Umali

Chakwera expresses gratitude to Muslim World League

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.