Malawi Broadcasting Corporation
Local News

Tigwire ntchito limodzi – Kamtukule

Nduna ya zokopa alendo, a Vera Kamtukule, yalimbikitsa anthu m’dziko muno kuti adzigwira ntchito limodzi ndi akatswiri a zachilengedwe pa ntchito yobzyala mitengo.

A Kamtukule ati izi ndi zofunika kaamba kakuti mitengo imafunika chisamaliro ikamakula, potwngeranso kuti anthu amadzala mitengo 10 million pa chaka koma 100,000 yokha ndiyo imakula.

Izi zinadziwika pa ntchito yobzyala mitengo kudera la mfumu yayikulu Maganga m’boma la Salima.

Related posts

Ministry of Water warns of potential floods in Southern Region

Romeo Umali

Mangochi Police hunts counterfeit

Romeo Umali

FAM president encourages Super League Coaches to embrace modern techniques

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.