Malawi Broadcasting Corporation
Africa Crime Local Local News Nkhani Politics

“Osanyoza anthu achikulire” — Chakwera

President Lazarus Chakwera wati khalidwe lonyoza anthu achikulire powanena kuti ndi mfiti ndi kuwapha (mob justice) zili ndi kuthekera kosokoneza ana achichepere m’dziko muno.

A Chakwera ati ndi pofunikanso kukhala ogwirizana, posatengera kusiyana zipani, zipembedzo ndi zina zambiri popeza anthu akakhala ogwirizana, dziko lino likhoza kupambana nkhondo yolimbana ndi njala.

#ChakweraDevelopmentalRally

Related posts

HOW WOMEN FARMERS IN MANGOCHI ARE TRANSFORMING THEIR LIVES THROUGH IRRIGATION AND SCHOOL FEEDING

McDonald Chiwayula

Mfumu yayikulu Mwirang’ombe yayamikira sukulu ya ntchito zaluso lamanja ku Karonga

Rabson Kondowe

WE ARE BACK WITH MBC ENTERTAINERS OF THE YEAR! STAY TUNED THIS EVENING!

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.