Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Tisunge bata, mtendere — Inkosi ya Makosi Goman V

Inkosi ya Makosi Gomani V ya m’boma la Ntcheu yati ili ndi chisoni chachikulu kaamba ka imfa ya Impi Bhiyeni Dr Saulos Chilima.

Inkosiyi yati Dr. Chilima anali mlangizi wa chingoni amene amamukonda, ndipo anali olimbikira, odzipereka ndi olimbikitsa chikhalidwe komanso odzipereka ku mpingo.

Iwo anayamikiranso khwimbi la anthu amene akupereka ulemu wawo otsiriza kwa malemu Dr. Chilima.

Koma iwo anati ngakhale aMalawi ali pa chisoni chachikulu, akuyenera kulimbikitsa mtendere.

Inkosi Ya Makosi Gomani yalangizanso aMalawi kuchita ndale zokomera dziko lonse.

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

Khumbize hails Lomola Health Post

MBC Online

Govt refutes 360% wage increase in State Residences

MBC Online

Amai atatu ali mchitokosi pamulandu wakuba ku Mangochi

Davie Umar
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.