Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Tisunge bata, mtendere — Inkosi ya Makosi Goman V

Inkosi ya Makosi Gomani V ya m’boma la Ntcheu yati ili ndi chisoni chachikulu kaamba ka imfa ya Impi Bhiyeni Dr Saulos Chilima.

Inkosiyi yati Dr. Chilima anali mlangizi wa chingoni amene amamukonda, ndipo anali olimbikira, odzipereka ndi olimbikitsa chikhalidwe komanso odzipereka ku mpingo.

Iwo anayamikiranso khwimbi la anthu amene akupereka ulemu wawo otsiriza kwa malemu Dr. Chilima.

Koma iwo anati ngakhale aMalawi ali pa chisoni chachikulu, akuyenera kulimbikitsa mtendere.

Inkosi Ya Makosi Gomani yalangizanso aMalawi kuchita ndale zokomera dziko lonse.

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

FOCCAD disburses K408 million to Improve livelihoods

MBC Online

Sheriffs seize Bullets’ bus over K25 million debt

MBC Online

Maranatha to award K5 million to top performing MSCE candidate

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.