Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

M’modzi wamwaliranso ndi ‘ambuye tengeni’, apolisi amanga atatu

Chiwerengero cha anthu omwe amwalira atamwa mowa odziwika kuti ‘ambuye tengeni’ kwa Manase ku Blantyre tsopano chafika pa asanu ndi atatu 8.

Apolisi atsimikiza kuti amanga anthu atatu kamba kankhaniyi.

MBC itatsatira nkhaniyi lero yapezanso kuti anthu ena awiri ali mwakayakaya pa chipatala chachikulu cha Queen Elizabeth pomwe munthu mmodzi amutulutsa atachira.

Related posts

Dedza MET worried over vandalism

Romeo Umali

CHAKWERA LAUNCHES 2022 AIP

MBC Online

Super League is developing, analysts say

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.