Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

M’modzi wamwaliranso ndi ‘ambuye tengeni’, apolisi amanga atatu

Chiwerengero cha anthu omwe amwalira atamwa mowa odziwika kuti ‘ambuye tengeni’ kwa Manase ku Blantyre tsopano chafika pa asanu ndi atatu 8.

Apolisi atsimikiza kuti amanga anthu atatu kamba kankhaniyi.

MBC itatsatira nkhaniyi lero yapezanso kuti anthu ena awiri ali mwakayakaya pa chipatala chachikulu cha Queen Elizabeth pomwe munthu mmodzi amutulutsa atachira.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Social Cash Transfer Programme transforms lives in Blantyre

Juliana Mlungama

ZAMBIRI MWA ZIMENE A CHAKWERA ANALONJEZA MU SONA YA 2023 ZACHITIKA – NDUNA

MBC Online

Malawi Police, NGOs partner to combat intimate partner violence

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.