Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

M’modzi wamwaliranso ndi ‘ambuye tengeni’, apolisi amanga atatu

Chiwerengero cha anthu omwe amwalira atamwa mowa odziwika kuti ‘ambuye tengeni’ kwa Manase ku Blantyre tsopano chafika pa asanu ndi atatu 8.

Apolisi atsimikiza kuti amanga anthu atatu kamba kankhaniyi.

MBC itatsatira nkhaniyi lero yapezanso kuti anthu ena awiri ali mwakayakaya pa chipatala chachikulu cha Queen Elizabeth pomwe munthu mmodzi amutulutsa atachira.

Related posts

DODMA rolls out food distribution exercise

Alinafe Mlamba

Northern police chief pledges more officers in Rumphi

Rabson Kondowe

Amugwira ataba makina opimila amayi apakati

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.