Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Young Stunna wafafaniza machimo ku Blantyre

Anthu amunzinda wa Blantyre anali okondwa kwambiri ataonelera maimbidwe ochititsa chidwi kuchoka kwa oimba wa chamba cha amapiano, Young Stunna, wochokera m’dziko la South Africa.

Mwambowu unali wachiwiri a Beerland and Classic Events atawukonzanso Young stunna atalephera kubwera m’mwezi wa May chaka chino.

Ena omwe anaimbanso kumwambowu anali Kell Kay, Eli Njuchi, Zeze Kingston, Tuno komanso Fada Moti.

Olemba: Andrew Lambulira

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

MEC, NICE intensify election awareness campaign

MBC Online

I am ready to face Popin — Chilemba

MBC Online

Amangidwa powaganizira kuti anapha munthu

Charles Pensulo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.