Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Sitima ya Marka itha kufika — Chithyola Banda

Sitima yochekera ku Beira m’dziko la Mozambique itha kufika ku Marka m’boma la Nsanje, atero a Chithyola Banda.

Nduna ya zachuma yi yatsindika kuti ntchito yokonza njanji ya sitima kuchoka ku Marka kufika ku Bangula yafika pamapeto, ndipo sitima itha kufika kuchoka ku Beira.

Iwo ayi izi zithandiza kupititsa chuma cha dziko lino patsogolo, maka kupyolera mu ntchito za malonda.

Related posts

Police urges collective efforts for festive season safety

Romeo Umali

PRESIDENTIAL PUBLIC PROGRAMME

MBC Online

Mzuzu City has a female Deputy Mayor

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.