Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Osagwiritsa ntchito imfa ya malemu Dr Chilima pa zifukwa za ndale’

Gulu lomwe likuzitcha ‘Mbadwa Zokhudzidwa’ lapempha anthu a ndale kuti asiye kugwiritsantchito imfa ya Dr Saulos Chilima pofuna kumema anthu kuti adziwakonda.

M’busa Thoko Banda, amene ndi m’modzi mwa akuluakulu a gululi amayankhula izi loweruka mu mnzinda wa Lilongwe ndipo anauza a Malawi kuti asiye kukhulupilira mabodza andale oterewa.

Mkulu winanso wa bungweli, a Billy Malata, anachenjeza a Malawi amene akufalitsa uthenga wabodza pa masamba a mchezo kuti azagamulidwa mlandu akawapeza.

A Malata analimbikitsanso chipani cha Malawi Congress (MCP) kuti chisachite ndale zonyoza.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

CHAKWERA TO ATTEND SEVENTH DAY ADVENTIST BLANTYRE CENTENARY CELEBRATIONS

McDonald Chiwayula

MANEPO yayamikira Madam Chakwera polimbana ndi nkhanza za anthu achikulire

Beatrice Mwape

WASTE MANAGEMENT INITIATIVES IMPRESS BCC

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.