Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Ndi mlandu kugulitsa, kuononga ndalama zachitsulo — Banki ya Reserve

Banki yayikulu m’dziko muno ya Reserve yati lamulo ligwira ntchito kwa anthu onse amene akugulitsa, kugula ndi kuononga ndalama za chitsulo.

Mu chikalata chomwe wasayinira ndi Gavanala wa bankiyi, a Wilson Banda, bankiyi yati olakwa adzilipira chindapusa chokwana K5 million.

M’sabata zapitazi, anthu ambiri akhala akutsatsa ndalama zachitsulo monga K5 ndi K10 ndipo zadziwika kuti anthuwa amasungunula ndi kuphwanya ndalamazi.

 

Related posts

Parliament to promote the wellbeing of women, children and adolescents

Rabson Kondowe

Climate Smart Programme participants receive wages

Romeo Umali

Malawi takes climate justice fight to ICJ

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.