Malawi Broadcasting Corporation
Environment Local Local News Nkhani

Kusowa kwa chakudya kwakula m’chigawo cha SADC

Chiwerengero cha anthu amene akukhudzidwa ndi bvuto losowa chakudya kaamba ka mavuto odza chifukwa cha kusintha kwa nyengo m’chigawo cha SADC chafika pa anthu 67.7 million kuchokera pa 57.1 million m’chaka cha 2023.

Izi ndi malinga ndi lipoti la akatswiri oona za nyengo m’chigawochi limene alitulutsa posachedwapa.

Akatswiriwa amayankhula izi pa msonkhano wawo womwe unachitika kuyambira pa 26 mpaka pa 28 August chaka chino.

Iwo amakumana pa chaka kawiri kuti agawane zomwe apeza pa zanyengo maka m’chigawo cha maiko akumwera muno mu Africa.

Olemba: Alufeyo Liyaya

Related posts

NBS Bank distances itself from Charity Shield Trophy presentation row

McDonald Chiwayula

Balaka turns out in voter registration despite mix-up

MBC Online

Norwegian govt committed to ensuring Malawians register for votes

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.