Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local News Nkhani

Mikozi ibweranso, eni ake atero

Mwini watsamba la mchezo la Mikozi, a Bright ‘Excess’ Chiligo, watsutsa mphekesera zimene zikumveka kuti tsamba lake anthu alichita chiwembu kuti lisowe pa makina a internet.

Chiligo wati tsambali libweleranso Lachisanu chifukwa pali ntchito imene akugwira yopanga tsambali kukhala lotetezeka kwa anthu achinyengo.

“Tawona kuti pa internet pachuluka masamba a mchezo amene akubera dzina lathu la Mikozi ndipo akumayika zinthu zoyipa,” iye anatero.

Anawonjezeranso kuti zimenezi zapangitsa kuti azilandira madandaulo ochuluka kuchokera kwa anthu.

 

Related posts

Region 5 to feature new sporting codes

Romeo Umali

Nkhata Bay, Rumphi to supply medical drugs through drones

Rabson Kondowe

Scotland drills Malawi Police on human rights protection

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.