Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local News Nkhani

Mikozi ibweranso, eni ake atero

Mwini watsamba la mchezo la Mikozi, a Bright ‘Excess’ Chiligo, watsutsa mphekesera zimene zikumveka kuti tsamba lake anthu alichita chiwembu kuti lisowe pa makina a internet.

Chiligo wati tsambali libweleranso Lachisanu chifukwa pali ntchito imene akugwira yopanga tsambali kukhala lotetezeka kwa anthu achinyengo.

“Tawona kuti pa internet pachuluka masamba a mchezo amene akubera dzina lathu la Mikozi ndipo akumayika zinthu zoyipa,” iye anatero.

Anawonjezeranso kuti zimenezi zapangitsa kuti azilandira madandaulo ochuluka kuchokera kwa anthu.

 

Related posts

JENDA POLICE APPREHEND 5 NOTORIOUS THIEVES

Romeo Umali

MODERN POST-HARVEST HANDLING METHOD REDUCING LOSSES

MBC Online

National Product Magazine urges stronger industry links to boost exports

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.