Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local Local News Nkhani

Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira

Mfumu yaikulu Nkhulambe ya m’boma la Phalombe yamwalira usiku wapitawu.

Malinga ndi bwanamkubwa wa boma la Phalombe, a Douglas Moffat, Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira itadwala kwa nthawi yochepa.

Pamenepa iwo ati ofesi yawo ndi akubanja akakambirana kuti akonze za tsiku limene ayike mmanda malemu mfumu yaikulu Nkhulambe.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Eye expert tells parents to limit children’s screen exposure

Chimwemwe Milulu

Mpulula displeased with Tigers’ performance in first round of TNM Super League

MBC Online

Boma la Neno lichita bwino polimbana ndi Edzi

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.