Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local Local News Nkhani

Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira

Mfumu yaikulu Nkhulambe ya m’boma la Phalombe yamwalira usiku wapitawu.

Malinga ndi bwanamkubwa wa boma la Phalombe, a Douglas Moffat, Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira itadwala kwa nthawi yochepa.

Pamenepa iwo ati ofesi yawo ndi akubanja akakambirana kuti akonze za tsiku limene ayike mmanda malemu mfumu yaikulu Nkhulambe.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Aphungu akufuna chamba chakwathu kuno chikhale chovomerezeka kulima

Madalitso Mhango

Dedza adds junior primary school

Sothini Ndazi

Analysts hail Chakwera’s cabinet reshuffle

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.