Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local Local News Nkhani

Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira

Mfumu yaikulu Nkhulambe ya m’boma la Phalombe yamwalira usiku wapitawu.

Malinga ndi bwanamkubwa wa boma la Phalombe, a Douglas Moffat, Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira itadwala kwa nthawi yochepa.

Pamenepa iwo ati ofesi yawo ndi akubanja akakambirana kuti akonze za tsiku limene ayike mmanda malemu mfumu yaikulu Nkhulambe.

 

Related posts

President Chakwera ayendera ntchito zachitukuko ku Mangochi

Romeo Umali

Introducing MBC’s WhatsApp channel and SMS news alert

Rabson Kondowe

Chipani cha ANC chikutsogola ku South Africa

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.