Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local Local News Nkhani

Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira

Mfumu yaikulu Nkhulambe ya m’boma la Phalombe yamwalira usiku wapitawu.

Malinga ndi bwanamkubwa wa boma la Phalombe, a Douglas Moffat, Mfumu yaikulu Nkhulambe yamwalira itadwala kwa nthawi yochepa.

Pamenepa iwo ati ofesi yawo ndi akubanja akakambirana kuti akonze za tsiku limene ayike mmanda malemu mfumu yaikulu Nkhulambe.

 

Related posts

President Chakwera wati atsogoleri a mipingo ali ndi ntchito yayikulu

Romeo Umali

JOSHUA MALANGO TROPHY PEGGED AT K15 MILLION

MBC Online

Phodo sips from Castel Cup

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.