Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Malawi, Tanzania akondwelera Kiswahili

Maiko a Malawi ndi Tanzania akuchita nawo mwambo okondwerera tsiku la chiyankhulo cha Kiswahili munzinda wa Lilongwe.

Mwambowu umachitika pofuna kulimbikitsa umodzi pakati pamaiko komanso chikhalidwe choyankhula ziyankhulo zosiyanasiyana pakati pa anthu.

Ena mwa amene ali kumeneku ndi monga kazembe wa dziko la Tanzania kuno ku Malawi, a Agness Kayola ndi nthumwi zawo.

Wachiwiri kwa kazembe wa dziko la Zimbabwe alinso komweku pamodzi ndi akuluakulu amu unduna owona za ubale wadzikolino ndi maiko ena, kuphatikizaponso ophunzira pa sukulu za ukachenjede.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Senaji in Kenya’s World Cup qualifier squad

MBC Online

Pikho Farms unveils the Kingstons as Mastercard Foundation ambassadors

Paul Mlowoka

MCP hails women support in strengthening the party

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.