Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Malawi, Tanzania akondwelera Kiswahili

Maiko a Malawi ndi Tanzania akuchita nawo mwambo okondwerera tsiku la chiyankhulo cha Kiswahili munzinda wa Lilongwe.

Mwambowu umachitika pofuna kulimbikitsa umodzi pakati pamaiko komanso chikhalidwe choyankhula ziyankhulo zosiyanasiyana pakati pa anthu.

Ena mwa amene ali kumeneku ndi monga kazembe wa dziko la Tanzania kuno ku Malawi, a Agness Kayola ndi nthumwi zawo.

Wachiwiri kwa kazembe wa dziko la Zimbabwe alinso komweku pamodzi ndi akuluakulu amu unduna owona za ubale wadzikolino ndi maiko ena, kuphatikizaponso ophunzira pa sukulu za ukachenjede.

 

Related posts

DODMA, UNDP push for disaster resilience

Rabson Kondowe

Anthu 1.4 million alowa nkaundula wa zipangizo zaulimi zotsika mtengo

Rabson Kondowe

From trash to treasure: Turning plastic waste into a source of income

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.